spot_img
16.8 C
New York
Saturday, May 18, 2024
spot_img

Mutharika Alonjeza Kukonzanso Malawi

Mtsogoleri wa chipani cha Democratic Progressive (DPP), Peter Mutharika walonjedza kukonza dziko lino lomwe akuti lawonongedwa ndi ulamuliro wa Lazarus Chakwera.

A Mutharika, omwenso akuzapikisana nawo pa chisankho cha mchaka cha mawa, anena izi kudzera pa tsamba lawo la mchezo lapa facebook.

Pamenepa, iwo apempha a Malawi kuti agwirane manja maka pokozanso dziko lowonongekali.

Mawu a Mutharika abwera pomwe kwangosala masiku ochepa kuti achititse msonkhano wa ndale mu mzinda wa Blantyre.

Mwa zina, iwo akuyembekezereka kufotokozera a Malawi mfundo zomwe akonza pokozanso dziko la Malawi.

Related Articles

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

- Advertisement -

Latest Articles