spot_img
spot_img
19.4 C
New York
Saturday, July 27, 2024
spot_img
spot_img

Mutharika Wasintha Thabwa: “Ndi muyankhulabe Chakwera mtsogolomu”

Mtsogoleri wachipani chotsutsa cha Democratic Progressive Party- (DPP) a Prerofessor Peter Mutharika wasintha thabwa pankhani yoti ayankhula a Malawi komanso President Lazarus Chakwera lero.

Lamulungu lapitali Mutharika, kudzera mmneneri wake bambo Shadrick Namalomba, anati alankhulapo pa nkhani zosiyanasiyana lero La Chitatu makamaka pa zautsogoleri wa Tonse.

Koma a Namalomba, mneneri wa Mutharika komanso chipani cha DPP, kudzera mu kalata ati mtsogoleri wakale wa dziko lino yu ayankhulabe mtsogolomu.

Related Articles

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

- Advertisement -

Latest Articles