spot_img
9.7 C
New York
Sunday, May 5, 2024
spot_img

BULU WATING’AMBA MNTHITI: Castel yakweza mtengo wa mowa

Bulu wating’amba mnthiti, wating’ambiranso zovala, Kampani ya Castel Malawi yakweza mtengo wa chakumwa chake chaukali chosiyanasiyana potsatira kutsika mphamvu kwa ndalama ya Kwacha.

Malinga ndi kalata yomwe kampaniyi yatulutsa yomwe wasayinira ndi mkulu wa zamalonda Johan Maree mitengo yatsopanoyi iyamba kugwira ntchito lero lachisanu pa 10 November.

Iwo afotokozanso kuti chakumwa chija cha Malawi Gin,Premier Brandy komanso Vodka mtengo wake sunasinthe ngakhale ndalama ya dziko linoyi yachepa mphamvu.

Related Articles

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

- Advertisement -

Latest Articles